Khristu Mu Nyimbo

No description added.

Chichewa 220 Songs

Uyang’ane Mdaniyo

[1]
Mkhristuwe dzuka! Alamula Mbuye;
Tenga cikopa, ndi lupanga m’dzanja,
Ukomane naye, usamuope
Ulimbe Mtima, Myang’ane mdaniyo.

Refrain:
Limba Mtima, Limba Mtima,
Limba Mtima, Pom’yang’ana mdani.

[2]
Zoopsa ziripo, ucenjeretu,
Usafulatire, ungapwekekwe;
Unyinji wa ’dani, udzagonjetsa,
Ulimbe Mtima, M’yang’ane mdaniyo.

[3]
Ntchito ya Mbuyako uiteteze;
Dzukatu mwa cangu nkhondoyo ithe;
Akakulamula, pita mwa cangu,
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo.

[4]
Pita limbikira, suli wekhai,
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Cikondi cace ngati mtsinje m’tengo;
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffee Buy us a coffee

Like this song


Share this song

Lyrics Videos on Youtube

AMAZING GRACE AMAZING GRACE Hymns Of Comfort
Wings Of A Dove Wings Of A Dove Golden Bells
Does Jesus Care Does Jesus Care Golden Bells
He Gave Me A Song He Gave Me A Song Songs On Request
Wade In The Water Wade In The Water Songs On Request
Joy To The World Joy To The World Caroling Songs