Loading Songs...

Kodi Yesu Asamala

[1]
Kodi Yesu asamalira
Nkasowa cimwemwe;
Ndikapsinjika ndi kuda nkhawa
M’njira yonse yaitari?

Chorus:
Ndidziwa amasamala, Inde ndikabvutika;
Ndithu masana ndi usiku amandisamalirane.

[2]
Kodi yesu asamalitsa
Mu’siku woopsa,
Pamene kwada zoopsa zadza,
Andisamalabe kodi?

[3]
Kodi Yesu asamalitsa
Ndikagwa m’mayeso?
Mwa za cisoni zosapumitsa,
Misozi usiku wonse?

[4]
Kodi Yesu asamalitsa
Poleka za dziko,
Ndiri kuthatha pafupi kufa
Kodi akundionadi?


Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

18 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

I WILL CALL UPON THE LORD I WILL CALL UPON THE LORD
Songs Of Prayer And Praise
Abide With Me Abide With Me
Golden Bells
A wonderful Saviour A wonderful Saviour
Spiritual Songs
GIVE THANKS GIVE THANKS
Songs Of Prayer And Praise
MARCHING TO ZION MARCHING TO ZION
Songs Of Prayer And Praise