Loading Songs...

Uyang’ane Mdaniyo

[1]
Mkhristuwe dzuka! Alamula Mbuye;
Tenga cikopa, ndi lupanga m’dzanja,
Ukomane naye, usamuope
Ulimbe Mtima, Myang’ane mdaniyo.

Refrain:
Limba Mtima, Limba Mtima,
Limba Mtima, Pom’yang’ana mdani.

[2]
Zoopsa ziripo, ucenjeretu,
Usafulatire, ungapwekekwe;
Unyinji wa ’dani, udzagonjetsa,
Ulimbe Mtima, M’yang’ane mdaniyo.

[3]
Ntchito ya Mbuyako uiteteze;
Dzukatu mwa cangu nkhondoyo ithe;
Akakulamula, pita mwa cangu,
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo.

[4]
Pita limbikira, suli wekhai,
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Cikondi cace ngati mtsinje m’tengo;
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS
Songs Of Prayer And Praise
Abide With Me Abide With Me
Golden Bells
Amazing Grace Amazing Grace
Golden Bells
Blessed Assurance Blessed Assurance
Christ In Song Hymnal
When The Roll Is Called Up Yonder When The Roll Is Called Up Yonder
Christ In Song Hymnal