Loading Songs...

Ulemu Kwa Mulungu

[1]
Ulemu kwa Mlungu, Ambuye Wathu, Ankonda, napatsa ’fe Mwana wace;
Napatsatu moyo kuombola ’fe, Pa khomo la moyo natsegulatu.

Chorus:
Tamani Mbuyeyo, Dziko limvere ’Ye; Tamani Mbuyeyo, Anthu akondwetu;
Idzani kwa Tate mwa Mwana wace, Mpatseni ulemu anaconda ’fe.

[2]
Anapulumutsa mwazi wace Amene akhulupririra mwa ’Ye.
Ngakhale wocimwa koposa ndithu, Adzakhulukidwa mwa YEsuyo.

[3]
Anatiphunzitsa zopambanazo, Tikondwa mwa Yesu, Ambuye wathu;
Komabe ’dzaziwa kopambanadi, Pamene atenga ’fe, kumwambako.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

5 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

I LOVE YOU LORD I LOVE YOU LORD
Songs Of Prayer And Praise
Moyo Wangu Sifu Bwana Moyo Wangu Sifu Bwana
Kiswahili Praise And Worship
Wade In The Water Wade In The Water
Songs On Request
He Gave Me A Song He Gave Me A Song
Songs On Request
Blessed Assurance Blessed Assurance
Christ In Song Hymnal
What A Friend We Have In Jesus What A Friend We Have In Jesus
Christ In Song Hymnal