Loading Songs...

Sindidzakusiya

[1]
Sindidzakusiya konse, Sindidzakukananso;
Ndzatsogola ndzakusunga, Mongwa mwa dzina langa;
Musaope coipaco, pomvera malangizo.

[2]
Mphepo zikaomba mkuntho, upemphere kwa Ine;
Ndidzakufungata iwe, Kukusamala bwino;
Poyesedwa konyazitsa, Ndidzakuyendetsa bwino.

[3]
Mlengalenga pong’azima pakakoma ponsepo,
Madyerero osasowa, Zokondweretsa zokha;
Ndidzakhala nawe ndithu, Ndi kuti usacimwe.

[4]
Ngati ndadodometsedwa, Ndi nkhawa ndi cisoni,
Ngakhaletu kuli nkhungu, Ndidzakuunikira,
Mbendera yokwezekayi, Ya cikondi canga njo.


Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy
Hillsong United
LORD OF ALL HOPEFULNESS LORD OF ALL HOPEFULNESS
Hymns Of Comfort
Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy
Christ In Song Hymnal
Amazing Grace Amazing Grace
Golden Bells
MARCHING TO ZION MARCHING TO ZION
Songs Of Prayer And Praise
BLESSED ASSURANCE BLESSED ASSURANCE
Songs Of Prayer And Praise