Loading Songs...

Sindidzakusiya

[1]
Sindidzakusiya konse, Sindidzakukananso;
Ndzatsogola ndzakusunga, Mongwa mwa dzina langa;
Musaope coipaco, pomvera malangizo.

[2]
Mphepo zikaomba mkuntho, upemphere kwa Ine;
Ndidzakufungata iwe, Kukusamala bwino;
Poyesedwa konyazitsa, Ndidzakuyendetsa bwino.

[3]
Mlengalenga pong’azima pakakoma ponsepo,
Madyerero osasowa, Zokondweretsa zokha;
Ndidzakhala nawe ndithu, Ndi kuti usacimwe.

[4]
Ngati ndadodometsedwa, Ndi nkhawa ndi cisoni,
Ngakhaletu kuli nkhungu, Ndidzakuunikira,
Mbendera yokwezekayi, Ya cikondi canga njo.


Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

How Great Thou Art How Great Thou Art
Spiritual Songs
Victory In Jesus Victory In Jesus
Golden Bells
I WILL SING OF THE MERCIES I WILL SING OF THE MERCIES
Hymns Of Comfort
Does Jesus Care? Does Jesus Care?
Spiritual Songs
He Gave Me A Song He Gave Me A Song
Songs On Request
Immortally Arrayed Immortally Arrayed
Songs On Request