Khristu Mu Nyimbo

No description added.

Chichewa 220 Songs

Nkhoswe Yadza

[1]
Lalikira mau konse kuli anthu
A mtima wosowa A m’dziko latsoka,
Mkhristu ali yense Anene mokondwa
Nkhoswe yafikadid!

Chorus:
Nkhoswe yafikadi, Nkhoswe yafikadi!
Mzimu wa Mulungu pangano la Mbuye;
Lalikira mau Konse kuli anthu,
Nkhoswe yafikadi!

[2]
Usiku wapiti, Kunja nako kwaca;
Kulira kwaleka, Ndi mkwiyo naonse,
Pamapiri napo Dzuwa lioneka;
Nkhoswe yafikadi!

[3]
Mfumu ya mafumu ibwera ndi mwayi,
Kwa ocimwa onse Kudzapulumutsa;
M’malomo mwa cete Mumveka nyimbo
Nkhoswe yafikadi!

[4]
Cikondi cakuya Ndicimene bwanji,
Kwa anthu ocimwa Apeze cisomo, Wocimwa ngati’ne Ndingawale bwanji;
Nkhoswe yafikadi!

[5]
Kuyimba kumveke Mlengalenga monse;
Oyera a m’mwamba Ndi a pansi pano
Abvomerezane Nyimbo yacikondi,
Nkhoswe yafikadi!



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffee Buy us a coffee

Like this song


Share this song

Lyrics Videos on Youtube

A wonderful Saviour A wonderful Saviour Spiritual Songs
WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS Songs Of Prayer And Praise
Glory Glory Songs On Request
DOES JESUS CARE? DOES JESUS CARE? Hymns Of Comfort
Jesus My Savior Jesus My Savior Songs On Request
Kutembea Nawe Kutembea Nawe Kiswahili Praise And Worship