Loading Songs...

Ndidzamdziwa Mombolo Wanga

[1]
Pamene nditatha zintchito zanga zonsezo,
Nditaoloka pa tsidya la nyanja;
Cakufaci cikadzabvalatu cosafanso;
Pompo ndidzamdziwa Mombolo wanga.

CHORUS:
Ndidzamudziwa, Ndidzamudziwa, Podzaima pa mbali pacepo,
Ndidzamudziwa, ndidzamudziwa, Ndi misomali m’manja mwace.

[2]
Moyo wanga udzakondwera pakumuona,
Ndi kuona nkhope yace yowala;
Ndidzamyamika Iye ndi mtima wanga wonse,
Malo adandikonzera kumwamba.

[3]
Ee! ndidzakondwa pakuona okondedwawo
omwe ndalekana nawo m’dzikoli;
Koma n’dzamba ndaonana naye Yesuyo,
Wokondedwa wanga wopambanayo.

[4]
Kupyolera pa zipata kunka ku mzindawo,
Iye adzanditsogolera ine,
Nyimbo ya nthawi zonse ndidzayimba mokondwa;
Nditamuona Mpulumutsi wanga.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

3 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Blessed Assurance Blessed Assurance
Spiritual Songs
ALL IN ALL ALL IN ALL
Songs Of Prayer And Praise
BLESSED ASSURANCE BLESSED ASSURANCE
Hymns Of Comfort
He Gave Me A Song He Gave Me A Song
Songs On Request