Khristu Mu Nyimbo

No description added.

Chichewa 220 Songs

’Mvani Yesu Aitana

[1]
’Mvani Yesu aitana, Ndani angagwiretu?
Mindayo yayera kale, Ndani akakunkhemo?
Momvekadi aitana, Mphotho ’dzalandira ’we
Ndani angayankhe msanga, Ndine Mbuye, tumeni.

[2]
Nkana sungapite mtari Ku maiko enawo,
Ungapeze anthu ena Apafupi ndi iwe.
Ngati sungalalikire mnga ngati Paulo,
Unganene za cikondi Ca Ambuye wakoyo.

[3]
Ngati sungakhale mlonga Wocenjeza anthuwo;
Kuwauza anthu njira yonka nayo mmwambamo;
Pakupempherera ena, Ungagwire ntchitoyo.
Ungacite ngati Huri pothangata Moseyo.

[4]
Mmene anthu alikufa, Mbuye aitanabe;
Wina asamamve nuti, singacite kanthui.
Gwira antchito wakupatsa, Nuigwire msangatu;
Ndi kuyankha poitana, Ndine Mbuye, tumeni.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffee Buy us a coffee

Like this song


Share this song

Lyrics Videos on Youtube

AMAZING GRACE AMAZING GRACE Hymns Of Comfort
Wings Of A Dove Wings Of A Dove Golden Bells
Does Jesus Care Does Jesus Care Golden Bells
He Gave Me A Song He Gave Me A Song Songs On Request
Wade In The Water Wade In The Water Songs On Request
Joy To The World Joy To The World Caroling Songs