Loading Songs...

Mulungu Atsogoza ’Ne

[1]
Mulungu atsogoza ’Ne, Ndapuma m’mtima mwangamo.
Ayang’anira m’njiramo, Poyenda ine konseko.

CHORUS:
Mulungu atsogoza ’ne, Ndi dzanja-dzanja lacelo.
Ndidzamtsatira Mbuyanga, Poyenda ine konseko.

[2]
Masiku ena mdima bi, Ndimabvutika m’mtimamo.
Pa nthawi zina nkondwadi, Popeza zokondwetsazo.

[3]
Ndzagwira dzanja lanulo, Osang’ung’udza konsei.
Ndidzaka mokondweratu, pomtsata Mbuye wangayo.

[4]
Podzatha ntchito yangayi, Podzagonjetsa chimolo.
Kumene ndidzakhalatu, Sindidzaopa imfayo.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

HOW GREAT THOU ART HOW GREAT THOU ART
Songs Of Prayer And Praise
When The Roll Is Called Up Yonder When The Roll Is Called Up Yonder
Christ In Song Hymnal
AMAZING GRACE AMAZING GRACE
Songs Of Prayer And Praise
Abide With Me Abide With Me
Christ In Song Hymnal
What A Friend What A Friend
Golden Bells