Loading Songs...

Msaiwale Tsiku La Mbuye

[1]
Msaiwale tsiku la Mbuye wathuyo.
Ndi tsiku lopambana masiku enawo;
Ndi tsiku lakupuma ndi la cimwemweco,
Kuwala kwace kuli kocoka mmwambamo.

CHORUS;
Tikondwera kudza kwa Sabata lacelo.
Tikondwera kudza kwa Sabata lacelo.

[2]
Sunga tsiku lace lopatulikalo,
Pembedza mwini njira yakunka mmwambamo;
Tikamtsatira Iye pa dziko linotu,
Adzatipatsa madzi a moyo wacewo.

[3]
Timyimbira Yesu pa tsiku lonseli,
Ambuye ali Bwenzi la ana onsewo.
Wokoma Mtima ndinu, Mukhale nafetu,
Munalonjeza kuti mudzadza mtimamu.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

1 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

I WILL CALL UPON THE LORD I WILL CALL UPON THE LORD
Songs Of Prayer And Praise
Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy
Christ In Song Hymnal
Blessed Assurance Blessed Assurance
Spiritual Songs
A wonderful Saviour A wonderful Saviour
Spiritual Songs