Loading Songs...

Mlungu Watisunga ’Fe

[1]
Mlungu watisunga ’fe Mpaka mlungu winawu;
T’yeni timpembedze ’Ye, Tsiku lopumali;
Tiganize zinthu za Mau a Mlunguyo.
Tiganize zinthu za Mau a Mulunguyo.

[2]
Pakufuna nsisizo, Zakudzera m’dzinalo,
Mudze, Mbuye wathu ’Nu, Mukhululukire ’fe;
Pakupuma mwanumo, Tikumbuka Inuyo.
Pakupuma mwanumo, Tikumbuka inuyo.

[3]
Pakulemekeza ’Nu, Tikuyandikira ’Nu;
Tikuona mphamvuyo, Ndi ulemererowo.
Mtithangate Mbuyathu Kudya phwando m’mwamba
Mtithangate Mbuyathu kudya pwando m’mwamba

[4]
Mbuye mugonjetsetu Chimo la mu mtimanga,
Kuti ndikagwiretu Ntchito zokondwetsa ’Nu.
Masabata onsewo Alingane momwemo,
Masabata onsewo Alingane momwemo.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

I WILL CALL UPON THE LORD I WILL CALL UPON THE LORD
Songs Of Prayer And Praise
When The Roll Is Called Up Yonder When The Roll Is Called Up Yonder
Christ In Song Hymnal
Ill Fly Away Ill Fly Away
Golden Bells
I LOVE YOU LORD I LOVE YOU LORD
Songs Of Prayer And Praise
GIVE THANKS GIVE THANKS
Songs Of Prayer And Praise