Maso Ndi Maso
[1]
Maso ndi maso ndi Khristu, Kodi ndidzachitanji?
Mmene ndidzaona Yesu, Yemwe anandifera
Chorus:
N’dzamona maso ndi maso, Kuseri kwa mitambo;
Posachedwa ndidzamona, Mulemerero wace!
[2]
Tsopano ndimona Iye, Mwa chizimezimetu,
Tsiku lija ndidzaona, Ulemerero wache.
[3]
Pamene zowawa zonse, Nthenda ndi imfa zitha,
Dziko likadzakonzedwa, Ndidzakondwa koposa.
[4]
Lodala tsikulo m’mene! Ndidzamuona Yesu,
Mpulumutsi wanga yemwe, Anandikonda ine.
Support Mysongbooks
Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.
Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.