Khristu Mu Nyimbo

No description added.

Chichewa 220 Songs

Kasupe Wa Madalitso

[1]
Idzani ndi madalitso, Mtima wanga uyimbe;
Nsisi zanu zisaleke, Kuti tiyamike ’Nu
Phunzitsani kumvera ’Nu, kuti ndikudziweni,
Pamene ciyembekezo Cidzaza Mtima wanga.

[2]
Ndinutu thandizo langa, Mwandifikitsa pano,
Ndipo mwa cifundo canu Ndikafika kwathuko.
Anandifuna Yesuyo, Posocera mtarimo;
Anakhetsa mwazi wace kundiombola ine.

[3]
M’ndipatse cisomo canu, Pakuti ndicisowa
Mundikokere kwa Inu Ndi cikondi canuno.
Sindifuna kusocera, Kukusiyani Inu
Tengani Mtima wangawu; Ukhale wanu konse


Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffee Buy us a coffee

Like this song


Share this song

Lyrics Videos on Youtube

Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy Hillsong United
AMAZING GRACE AMAZING GRACE Hymns Of Comfort
Ancient Words Ancient Words Golden Bells
Blessed Assurance Blessed Assurance Christ In Song Hymnal