Loading Songs...

Kasupe Wa Madalitso

[1]
Idzani ndi madalitso, Mtima wanga uyimbe;
Nsisi zanu zisaleke, Kuti tiyamike ’Nu
Phunzitsani kumvera ’Nu, kuti ndikudziweni,
Pamene ciyembekezo Cidzaza Mtima wanga.

[2]
Ndinutu thandizo langa, Mwandifikitsa pano,
Ndipo mwa cifundo canu Ndikafika kwathuko.
Anandifuna Yesuyo, Posocera mtarimo;
Anakhetsa mwazi wace kundiombola ine.

[3]
M’ndipatse cisomo canu, Pakuti ndicisowa
Mundikokere kwa Inu Ndi cikondi canuno.
Sindifuna kusocera, Kukusiyani Inu
Tengani Mtima wangawu; Ukhale wanu konse


Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

5 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

God Bless You, Go With God God Bless You, Go With God
Songs On Request
HOLY HOLY HOLY HOLY HOLY HOLY
Songs Of Prayer And Praise
Blessed Assurance Blessed Assurance
Christ In Song Hymnal
WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS WHAT A FRIEND WE HAVE IN JESUS
Songs Of Prayer And Praise
Moyo Wangu Sifu Bwana Moyo Wangu Sifu Bwana
Kiswahili Praise And Worship
I Sing The Mighty Power I Sing The Mighty Power
Christ In Song Hymnal