Loading Songs...

Akristu Tiyeni

[1]
Akristu tiyeni! Nkhondo tigwira,
Yesu Mbuye wathu, Atitsogoza,
Ona mbuye yekha, Atithanziza;
Ndi mbendera yace, Tiyitsatira.

CHORUS
Akristu tiyeni! Nkhondo tigwire,
Yesu Mbuye wathu, Atitsogoza.

[2]
Nkhondo ya Satana, Msanga ithawa,
Akristu tiyeni, Tidzapambana;
Mphamvu zace zitha, Yesu titama;
Timbani anzathu Nyimbo tikweza.

[3]
Gulu larikulu, Adza Akristu;
Titsatana namwo, Ana a Mlungu;
Sitipatukana, Tonse tikhala,
ndi mtima umodzi, Timakondana.

[4]
Zonse za pa dziko, Zidzatheratu;
Koma mpingo wace, Ukhalitsabe;
Mphamvu ya Satana, idzalefuka;
Yesu nalonjeza ndidzalimbitsa.

[5]
Idzani Akristu, Kutithandiza,
Nyimbo za Mulungu, tidzayimbitsa;
Kristu ayenera, Ndiye Mfumuyo,
Tidzalemekeza, Nthawi zonsezo.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

5 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Listen To Our Hearts Listen To Our Hearts
Songs On Request
Amazing Grace Amazing Grace
Golden Bells
Immortally Arrayed Immortally Arrayed
Songs On Request
Does Jesus Care? Does Jesus Care?
Christ In Song Hymnal
Joy to the World Joy to the World
Sunday School Songs
God Bless You, Go With God God Bless You, Go With God
Songs On Request