Loading Songs...

Yesu Mundilankhule

[1]
Yesu, Mundilankhule, Mau ofatsawo;
Mndinong’oneze kuti, SUlitu wekha ’we.
Mtima munditsegule, Kuti ndimvere ’Nu;
Mdzaze mu Mtima wanga, Kuti ndikondwedi.

Chorus:
Mundinong’onezetu, mwa nsisi zanuzo
Udzagonjetsa ndithu, Udzamasukadi.
Mundilankhule, Mbuye, Tsiku ndi tsikunso,
Ndimvetu mau anu, Sulita wekha ’we

[2]
Yesu, munene mau Ndi ana anuwo,
Kuyang’anira Inu, Muwapjunzitsetu;
Kuti apereketu Moyo kwa inuyo,
Udze ufumu wanu, Kuti ’dzaone ’Nu.

[3]
Kale munaonetsa Kufuna kwanuko,
Yanga ndidziwe ntchito, Ndicite zanuzo;
Ndilemekeze Inu, Kwa anthu onsewo,
Ncite kufuna kwanu, Masiku onsewo.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

2 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Ancient Words Ancient Words
Golden Bells
Here I Am To Worship Here I Am To Worship
Hillsong United
What A Friend What A Friend
Golden Bells
I LOVE YOU LORD I LOVE YOU LORD
Songs Of Prayer And Praise
Hide Me, Rock Of Ages Hide Me, Rock Of Ages
Songs On Request