Loading Songs...

Uyang’ane Mdaniyo

[1]
Mkhristuwe dzuka! Alamula Mbuye;
Tenga cikopa, ndi lupanga m’dzanja,
Ukomane naye, usamuope
Ulimbe Mtima, Myang’ane mdaniyo.

Refrain:
Limba Mtima, Limba Mtima,
Limba Mtima, Pom’yang’ana mdani.

[2]
Zoopsa ziripo, ucenjeretu,
Usafulatire, ungapwekekwe;
Unyinji wa ’dani, udzagonjetsa,
Ulimbe Mtima, M’yang’ane mdaniyo.

[3]
Ntchito ya Mbuyako uiteteze;
Dzukatu mwa cangu nkhondoyo ithe;
Akakulamula, pita mwa cangu,
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo.

[4]
Pita limbikira, suli wekhai,
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Cikondi cace ngati mtsinje m’tengo;
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

0 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Hide Me, Rock Of Ages Hide Me, Rock Of Ages
Songs On Request
ABIDE WITH ME ABIDE WITH ME
Hymns Of Comfort
AMAZING GRACE AMAZING GRACE
Hymns Of Comfort
Servant’s Song Servant’s Song
Songs On Request
I LOVE YOU LORD I LOVE YOU LORD
Songs Of Prayer And Praise
Aliyeniokoa Aliyeniokoa
Kiswahili Praise And Worship