Loading Songs...

Masika A Dziko Ayandika

[1]
Masika a dziko ayandikatu, Aitana Mbuye okololawo;
Ndi mina yeyera pa dziko lonse, Ndi mwini zotuta wayandikanso.

Chorus:
’Dzanitu msanga, Tengatu zotuta; Mdzatitengae ’fe, Kwathuko

Alto, Tenor, ndi Bass;
Idzanitu angelo, msangatu; Tengereni zotuta mmwambamo.
Mudzatengetu ife, kunkatu, Kwathu mmwambamo.

[2]
E, tsiku lopanda misozi konse, Layandika kudza mothamangatu;
Akubalalika ndi ucimowo, Mwasonkhetu nthawi isanathei.

[3]
Ikomatu ntchito ya cikondico, Kasupe wosaphwa wa kumwambako;
Cikonditu ndico ciitana ’fe, Cigwiritsa ntchito, Cibalitsatu.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

2 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

A wonderful Saviour A wonderful Saviour
Spiritual Songs
Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy
Christ In Song Hymnal
He Hideth My Soul He Hideth My Soul
Golden Bells
I Sing The Mighty Power I Sing The Mighty Power
Christ In Song Hymnal
Sing The Wondrous Love Sing The Wondrous Love
Spiritual Songs
ABIDE WITH ME ABIDE WITH ME
Hymns Of Comfort