Loading Songs...

Idza Tsiku Lopuma

[1]
Idza tsiku lopma, Lopatsidwa ku dziko.
Idza mmtima mwangamu, Monga nyali ya mmwamba.

[2]
Tsiku lokondweretsa, Likupita msangatu;
Litisangalatsanso Mpaka ntchito idzatha.

[3]
Tsiku l oyeretsetsa, Tsiku lakupemphera;
Tsiku lakulandira madalitso anuwo.

[4]
Idza tsiku lopma ndi zimphamvu za mmwamba,
Ndi kuyera kwanuko Kudze m’mtima mwangamu.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

1 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

What A Friend What A Friend
Golden Bells
BLESSED ASSURANCE BLESSED ASSURANCE
Songs Of Prayer And Praise
Victory In Jesus Victory In Jesus
Golden Bells
Come Unto Me Come Unto Me
Christ In Song Hymnal
Abide With Me Abide With Me
Golden Bells