Loading Songs...

Khalatu Woyera

[1]
Khalatu woyera, Pemphera mtseri;
Werenga mau ’ce, Masiku once;
Thangatani omwe Ali ofo’oka,
Madalitso ace Funanani.

[2]
Khalatu woyera, Dziko laipa;
Pemphera kolimba, Kwa Yesu Mbuye;
Yang’anitsa Yesu, Ndi Kumtsatira
Kuti anthu ena, Aone Yesu.

[3]
Khalatu woyera, Akutsogoze,
Usamtsogolere, m’njira zakozo;
M’nsoni ndi pokondwa, Tsata Mbuyako
Khulupira Yesu Ndi mau ace.

[4]
Khalatu woyera, Khala wofatsa,
Alamulire ’Ye, Ganizo lako;
Utatsogozedwa Ndi Mzimu wace,
Msanga udzagwira Ntchito ya mmwamba.



Support Mysongbooks

Support us by joining the Buy Me A Coffee community and making a small donation, you can help us expand our library and ensure that music lovers everywhere can enjoy their favorite songs to the fullest. We're passionate about music, and we know you are too, so let's work together to keep the music alive.

Thank you for being a part of our community and supporting our mission to provide the best lyrics library on the internet.

Buy me a coffeeBuy us a coffee

Like this song

1 Likes

Share this song

Facebook WhatsApp Twitter Telegram LinkedIn Email

Lyrics Videos on Youtube

Holy, Holy, Holy Holy, Holy, Holy
Christ In Song Hymnal
Amazing Grace Amazing Grace
Golden Bells
ALL IN ALL ALL IN ALL
Songs Of Prayer And Praise
God Bless You, Go With God God Bless You, Go With God
Songs On Request
Come Unto Me Come Unto Me
Christ In Song Hymnal